Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g89 8/8 tsamba 10
  • Sitolo Yochedwetsedwa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Sitolo Yochedwetsedwa
  • Galamukani!—1989
  • Nkhani Yofanana
  • Kulalikira Pamsika
    Nsanja ya Olonda—2008
  • N’chifukwa Chiyani Timamanga Nyumba za Ufumu Ndipo Timazimanga Bwanji?
    Kodi Ndani Akuchita Chifuniro cha Yehova Masiku Ano?
  • Ntchito Yomanga Yomwe Imalemekeza Yehova
    Ufumu wa Mulungu Ukulamulira
  • Mmene Anthu Akuwonjezekera Pakufunika Nyumba Zina Mwamsanga
    Nsanja ya Olonda—2002
Onani Zambiri
Galamukani!—1989
g89 8/8 tsamba 10

Sitolo Yochedwetsedwa

Chithunzithunzi choseketsa cholembedwa posachedwapa mu “Scranton Times,” ya Scranton, Pennsylvania, chinapanga ndemanga ponena za kuchedwetsedwa kotalika kwa tauniyo kumaliza makonzedwe kaamba ka sitolo yogulako zinthu. Chithunzithunzi chimodzi chinanena kwa chinzake kuti: “Chikuwoneka ngati chikutenga nthaŵi yosatha kuyamba sitoloyo!” chinacho chinayankha kuti: “Iwo ayenera kuitcha iyo ‘Sitolo ya Nyumba ya Ufumu!’ Mboni za Yehova zidzaimanga iyo m’masiku 3!”

M’maiko ambiri Mboni za Yehova zikudziŵidwa mofala kaamba ka mazana angapo a Nyumba za Ufumu zawo zomangidwa mofulumira. Iwo ali ndi magulu omanga ophunzitsidwa mwapadera ndi kulinganiza kwabwino kwapasadakhale. Monga chotulukapo, Nyumba za Ufumu zikumangidwa kuchokera m’maora 30 kufikira masiku 4. Ndipo anthu akuchiwona icho.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena