Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g92 10/8 tsamba 31
  • Kutetezera Ana Kunkhalwe, 1882

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kutetezera Ana Kunkhalwe, 1882
  • Galamukani!—1992
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Nkhanza Zidzathadi?
    Nsanja ya Olonda—2007
  • Dikirani Moleza Mtima
    Nsanja ya Olonda—1998
  • Chiyembekezo Chenicheni kwa Ana
    Galamukani!—1994
  • Zomwe Munganene Pogawira Magazini
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2007
Onani Zambiri
Galamukani!—1992
g92 10/8 tsamba 31

Kutetezera Ana Kunkhalwe, 1882

“GULU LOTETEZERA ANA KUNKHALWE, 1882. Gulu Lotetezera Ana Kunkhalwe linayambidwa mu New York mu 1875 ndi Henry Bergh. Zaka zisanu ndi ziŵiri pambuyo pa kuyambidwa kwake, Gulu limeneli, limene liri gulu loyamba kupereka chitetezo chirichonse kwa ana ochitiridwa nkhanza mumzinda [wa New York], linali kusamalira madandaulo zikwi zambiri chaka chirichonse, kuchotsa ana m’mabanja osayenera ndi kulanga olakwa kupyolera mwa mabwalo amilandu. Chithunzithunzi chozokotedwa mwatanthauzo chimenechi chikuimira kuphatikizidwa kwapanthaŵi yake kwa maulamuliro m’nkhaniyo.”—New York in the Nineteenth Century, lolembedwa ndi John Grafton.

[Mawu a Chithunzi patsamba 31]

New York in the Nineteenth Century, lolembedwa ndi John Grafton, Dover Publications, Inc.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena