Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g00 2/8 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2000
  • Nkhani Yofanana
  • Mabanja Opanda Bambo—Chizindikiro cha Nthaŵi
    Galamukani!—2000
  • Atate wa Ana Amasiye
    Nsanja ya Olonda—2009
  • Mafunso Ochokera kwa Oŵerenga
    Nsanja ya Olonda—1994
  • Mmene Vuto la Mabanja Opanda Bambo—Lingathetsedwere
    Galamukani!—2000
Onani Zambiri
Galamukani!—2000
g00 2/8 tsamba 1-2

Zamkatimu

February 8, 2000

Mmene Vuto la Mabanja Opanda Bambo Lingathetsedwere 3-11

Ana ochulukirachulukira akuleredwa popanda abambo. Kodi chikuchititsa vuto losautsali n’chiyani? Kodi mabanja angathandizidwe bwanji kuti akhalebe olimba?

3 Mabanja Opanda Bambo—Chizindikiro cha Nthaŵi

4 Chifukwa Chimene Abambo Akusoŵera

8 Mmene Vuto la Mabanja Opanda Bambo—Lingathetsedwere

12 Anthu Ovutika ndi Nkhondo Asintha

13 Kusiyana Pakati pa Olemera ndi Osauka Kukukula

22 Mliri wa Matenda a Makoswe—Unakantha Ulaya M’Nyengo Zapakati

25 Kupanga Mapu Osonyeza Miyamba—M’nthaŵi Zakale Ndiponso Tsopano

28 Lingaliro la Baibulo

Kunama—Kodi Nthaŵi Zina N’kolungama?

26 Kamzimbi—Mbalame Yokongola kwambiri

32 ‘Linandithandiza Kupenda Moyo Wanga’

Kodi Ndingapeŵe Bwanji Zoopsa pa Intaneti? 19

Achinyamata ambiri akugwiritsa ntchito Intaneti. Kodi ndi motani mmene angagwiritsire ntchito mwanzeru chida champhamvu chimenechi?

Kumeta Moyeretsa 22

Tsiku ndi tsiku amuna padziko lonse amameta ndevu zawo. Kodi mbiri yometa ndevu ili yotani? Ndipo kodi mungamete bwanji moyeretsa?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena