Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g05 11/8 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2005
  • Nkhani Yofanana
  • Mwetulirani—N’zothandiza kwa Inu!
    Galamukani!—2000
  • Ubwino wa Kumwetulira
    Galamukani!—2003
  • Kumwetulira Ndi Mphatso Yofunika Kugawana
    Galamukani!—2017
  • Limbikitsani Osauka
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2007
Onani Zambiri
Galamukani!—2005
g05 11/8 tsamba 1-2

Zamkatimu

November 8, 2005

Kodi Osauka Angayembekezere Zotani?

Akuti anthu okhala padziko lapansi ndi ogawikana pawiri, olemera ndi osauka. Popeza anthu osauka akuchulukirachulukira, kodi angayembekezere zotani?

3 Dziko Logawanika Chifukwa cha Chuma

4 Kusiyana Kwakukulu Pakati pa Olemera ndi Osauka

7 Njira Yeniyeni Yothetsera Umphawi

16 Zimene Achinyamata Amadzifunsa

Kodi Ndingapewe Bwanji Mavuto Pocheza ndi Anthu Osawadziwa pa Intaneti?

19 Mphamvu Zimene Manyuzipepala Ali Nazo

20 Kuuza Anthu Nkhani

7 Mmene Mungapindulire ndi Manyuzipepala

27 Malo Ovuta Kuwamvetsa a ku Africa

28 Zimene Baibulo Limanena

Kodi Baibulo Limapondereza Akazi?

26 “Tikakumane Pachitsime”

26 Mayankho Othandiza a Mafunso Amene Mwakhala Mukufunsa

Nkhondo Imene Inasintha Moyo Wanga 11

Msilikali wa m’gulu la asilikali apamadzi wa ku United States amene anapita ku malo omenyerana nkhondo nthawi 284 pankhondo ya ku Vietnam ndipo analandira mamendulo 29 akufotokoza momwe nkhondo imeneyo inasinthira moyo wake.

Kodi Baibulo Limapondereza Akazi? 28

Anthu ambiri amati zimene Baibulo limaphunzitsa, zoti akazi azigonjera amuna n’zopondereza akazi. Kodi zimenezi n’zoona?

[Mawu a Chithunzi patsamba 2]

Cover: © Karen Robinson/Panos Pictures

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena