Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 1/09 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2009
  • Nkhani Yofanana
  • Mlomo wa Mbalame Yotchedwa Toucan
    Galamukani!—2009
  • Kodi Padzikoli Madzi Akutha?
    Galamukani!—2001
  • Zimene Anthu Akuchita Pofuna kuthetsa Vuto la Kusowa kwa Madzi
    Galamukani!—2009
  • Kumene Kuli Mavuto Aakulu
    Galamukani!—1997
Onani Zambiri
Galamukani!—2009
g 1/09 tsamba 1-2

Zamkatimu

January 2009

Madzi Akutha Padzikoli?

Chaka chilichonse anthu mamiliyoni ambiri amafa chifukwa cha uve komanso kumwa madzi oipa. Kodi pali njira iliyonse yothetsera vutoli?

3 Kodi Madzi Akutha Padzikoli?

5 Zimene Anthu Akuchita Pofuna Kuthetsa Vuto la Kusowa kwa Madzi

8 Madzi Opatsa Moyo

12 Tinapeza Zimene Tinkafuna

17 Panagona Luso

Mlomo wa Mbalame Yotchedwa Toucan

18 Zimene Achinyamata Amadzifunsa

Kodi Ndithetse Chibwenzi?

21 Anthu Otcheza Mchere ku Sahara

24 Akapolo Oiwalidwa a ku South Pacific

26 Anthu Ambiri Amakonda Pizza

30 Zochitika Padzikoli

31 Kodi Mungayankhe Bwanji?

32 Kodi Mulungu Amatisamaliradi

Kuthandiza Ana Amene Ali ndi Vuto Lophunzira 10

Kodi mungatani ngati mwana wanu ali ndi vuto lolephera kuwerenga kapena kuphunzira zinthu zina?

Kodi Tikamavutika Ndiye Kuti Mulungu Akutilanga? 28

Kodi mukamakumana ndi mavuto ndiye kuti Mulungu akunyansidwa nanu?

[Chithunzi patsamba 2]

Anthu akutunga madzi pa chitsime chachikulu, kutachitika chilala choopsa m’dera la Gujarat, ku India

[Mawu a Chithunzi]

REUTERS/Amit Dave

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena