Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g21 No. 3 tsamba 16
  • Fufuzani Umboni

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Fufuzani Umboni
  • Galamukani!—2021
  • Nkhani Yofanana
  • Muzithandiza Ana Anu Kuti Azikhulupirira Kwambiri Mlengi
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Kodi Moyo Unayamba Bwanji?
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
  • Muzikhulupirira Kwambiri Mlengi
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • Gwiritsani Ntchito Kabuku Kakuti Uthenga Wabwino Wochokera kwa Mulungu
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
Onani Zambiri
Galamukani!—2021
g21 No. 3 tsamba 16
Wachinyamata ali mu laibulale ndipo akuwerenga kabuku kakuti “Kodi Zamoyo Zinachita Kulengedwa?” pa tabuleti yake.

Fufuzani Umboni

Magazini ya Galamukani! ino ikufotokoza maumboni ena amene amasonyeza kuti zinthu zam’chilengedwechi zinachita kulengedwa. Fufuzani umboni umenewu ndipo onani ngati pali zifukwa zomveka zimene zingakuchititseni kukhulupirira kuti kuli Mlengi. M’munsimu, muli mitu ya mavidiyo komanso mabuku ena amene angakuthandizeni kupeza mfundo zina zothandiza. Mungapeze mitu imeneyi pa jw.org.

N’chifukwa chiyani anthu ambiri ophunzira amakhulupirira kuti kuli Mlengi?

Onerani zimene ena anafotokoza pa mavidiyo akuti Zokhudza Mmene Moyo Unayambira.

Kodi pali mfundo zomveka zotsimikizira kuti zamoyo zinachita kusintha?

Werengani kabuku kakuti Kodi Zamoyo Zinachita Kulengedwa?

Kodi n’zomveka kukhulupirira kuti kuli Mlengi?

Onerani vidiyo yakuti Zimene Achinyamata Anzanu Amanena—Kukhulupirira Kuti Kuli Mulungu.

Kodi ndi nzeru kukhulupirira Baibulo?

Werengani kabuku kakuti Mmene Moyo Unayambira—Mafunso 5 Ofunika Kwambiri.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena