Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mb phunziro 6
  • Phunziro 6

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Phunziro 6
  • Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
  • Nkhani Yofanana
  • Tinapangidwa Modabwitsa Kwambiri
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Yehova Amatidziŵa Bwino!
    Nsanja ya Olonda​—1990
  • Phunziro 5
    Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
  • Phunziro 1
    Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
Onani Zambiri
Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
mb phunziro 6

Phunziro 6

Losindikizidwa
Losindikizidwa

Salimo 139:14

Tayang’ana zala zako za m’manjazo ndipo ugwedeze zala zako za kumiyendo.

Loza makutu ako, kenako uloze mphuno yako.

Tayang’ana miyendo yakoyo. Miyendo imeneyi ndi yomwe imakuthandiza kuti uzitha kuthamanga, kudumpha, kupanga masewera ozungulira ndi masewera ena osiyanasiyana.

Yang’ana pagalasi. Kodi ukuona chiyani?

Zonse zimene Yehova anapanga n’zabwino kwambiri.

ZOTI MUCHITE

Mwana wanuyo muwerengereni:

Salimo 139:14

Muuzeni mwanayo kuti aloze:

Zala zake zam’manja Zala zake zakumiyendo Mphuno yake

Makutu ake Pakamwa pake

Pezani zinthu zobisika.

Nkhanu Mphaka

Mufunseni mwana wanu kuti:

Kodi ndani analenga iweyo ndi ine?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena