Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • snnw tsamba 3
  • Inu Ndinu Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Inu Ndinu Yehova
  • Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Yofanana
  • ‘Dzina Lanu Ndi Yehova’
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Athandizeni Kukhala Olimba
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Moyo wa Mpainiya
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw tsamba 3

Nyimbo 138

Inu Ndinu Yehova

(Salimo 83:18)

  1. Mulungu woona

    Wachilengedwe chonse

    Mulungu wamuyaya

    Ndinudi Yehova.

    Ndifetu amwayi

    Kukhala anthu anu

    Tilalika za inu,

    Ku mitundu yonse.

    (KOLASI)

    Yehova, Yehova,

    M’lungu ndinu nokha

    Kumwambako ndi padziko.

    Palibenso wina

    Ndinudi Wamphamvuyonse

    Onsetu adziwe

    Yehova, Yehova,

    M’lungu wathu ndinu nokha.

  2. Tingathe kukhala,

    Chilichonse mwasankha.

    Tigwire ntchito yanu

    Ndinudi Yehova

    Mwatipatsa dzina

    Tikhale Mboni zanu

    Uwu ndi mwayi wathu

    Tikutamandani

    (KOLASI)

    Yehova, Yehova,

    M’lungu ndinu nokha

    Kumwambako ndi padziko.

    Palibenso wina

    Ndinudi Wamphamvuyonse

    Onsetu adziwe

    Yehova, Yehova,

    M’lungu wathu ndinu nokha.

(Onaninso 2 Mbiri 6:14; Sal. 72:19; Yes. 42:8.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena