Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 76
  • Kodi Mumamva Bwanji?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mumamva Bwanji?
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mumamva Bwanji?
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nyimbo kwa Wammwambamwambayo
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Yehova Akutipempha Kuti: “Mwana Wanga Khala Wanzeru”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • “Muzitha Kusankha Zinthu Zimene Ndi Zofunikadi Kwambiri”
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 76

NYIMBO 76

Kodi Mumamva Bwanji?

Losindikizidwa

(Aheberi 13:15)

  1. 1. Kodi m’mamva bwanji

    Mukasonyeza khama

    Polalikira anthu

    Ndi kuwaphunzitsa?

    Mukamayesetsa

    M’lungu adzadalitsa.

    Mudzathandiza anthu

    Kudziwa Mulungu.

    (KOLASI)

    Timasangalala ndithu

    Kupereka mtima wathu,

    Choncho timutumikire

    Tsiku lililonse.

  2. 2. Kodi m’mamva bwanji

    Mukadziwatu kuti

    Mwawafika pamtima

    Akamva uthenga?

    Ena amakana,

    Ena amatitsutsa.

    Koma timanyadira

    Tikalalikira.

    (KOLASI)

    Timasangalala ndithu

    Kupereka mtima wathu,

    Choncho timutumikire

    Tsiku lililonse.

  3. 3. Kodi m’mamva bwanji

    Pokumbukira kuti

    Mwa chikondi Yehova

    Amatsogolera?

    Timalalikira,

    Timaphunzitsa anthu

    Akhale ndi tsogolo,

    Adzapeze moyo.

    (KOLASI)

    Timasangalala ndithu

    Kupereka mtima wathu,

    Choncho timutumikire

    Tsiku lililonse.

(Onaninso Mac. 13:48; 1 Ates. 2:4; 1 Tim. 1:​11.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena