Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • rr tsamba 28-29
  • “Kumwamba Kunatseguka”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Kumwamba Kunatseguka”
  • Yehova Wabwezeretsa Kulambira Koyera
  • Nkhani Yofanana
  • “Ndidzakhala Pakati pa Aisiraeli”—Yehova Wabwezeretsa Kulambira Koyera
    Yehova Wabwezeretsa Kulambira Koyera
  • Mafunso Okhudza Mmene Zilili Kumwamba
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2016
  • Zimene Zinachitika Yesu Asanayambe Utumiki Wake
    Yesu—Ndi Njira, Choonadi ndi Moyo
  • ‘Ndidzakusonkhanitsani Pamodzi’—Mulungu Analonjeza Kuti Adzabwezeretsa Kulambira Koyera
    Yehova Wabwezeretsa Kulambira Koyera
Onani Zambiri
Yehova Wabwezeretsa Kulambira Koyera
rr tsamba 28-29
Ezekieli akuona galeta la Yehova limene likutsika ndi mphepo yamphamvu.

GAWO 1

“Kumwamba Kunatseguka”

EZEKIELI 1:1

MFUNDO YAIKULU: Tiona mwachidule zokhudza kumwamba kumene Yehova amakhala

Palibe munthu amene angaone Yehova, Mulungu wamphamvuyonse n’kukhalabe ndi moyo. (Eks. 33:20) Koma Yehova anaonetsa Ezekieli masomphenya amene amatithandiza kudziwa mbali yakumwamba ya gulu lake. Masomphenya amenewa amatichititsa mantha komanso amatipangitsa kuti tiziyamikira kwambiri mwayi umene tili nawo wolambira Mulungu woona.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena