Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • CA-brpgm18 tsamba 3-4
  • Muzimvetsera Mwachidwi Kuti Mupeze Mayankho a Mafunso Awa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzimvetsera Mwachidwi Kuti Mupeze Mayankho a Mafunso Awa
  • Pulogalamu ya Msonkhano Wadera ya 2017-2018—Womwe Padzakhale Woimira Nthambi
  • Nkhani Yofanana
  • Mafunso Ochokera Kwa Owerenga
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • Chimene Chilamulo cha Mose Chimatanthauza kwa Inu
    Ogwirizana m’Kulambiridwa kwa Mulungu Yekha Wowona
  • Chilamulo cha Kristu
    Nsanja ya Olonda—1996
  • Kutsatira Chilamulo cha Kristu
    Nsanja ya Olonda—1996
Onani Zambiri
Pulogalamu ya Msonkhano Wadera ya 2017-2018—Womwe Padzakhale Woimira Nthambi
CA-brpgm18 tsamba 3-4

Muzimvetsera Mwachidwi Kuti Mupeze Mayankho a Mafunso Awa:

  1. Kodi “chilamulo cha Khristu” n’chiyani? (Agal. 6:2)

  2. Kodi tingakwaniritse bwanji chilamulo cha Khristu ngakhale pamene anthu ena sakutiona? (1 Akor. 10:31)

  3. Kodi timakwaniritsa bwanji chilamulo cha Khristu tikamalalikira? (Luka 16:10; Mat. 22:39; Mac. 20:35)

  4. N’chifukwa chiyani tinganene kuti chilamulo cha Khristu ndi chabwino kwambiri kuposa Chilamulo cha Mose? (1 Pet. 2:16)

  5. Kodi anthu apabanja komanso makolo angatani kuti azikwaniritsa chilamulo cha Khristu m’banja mwawo? (Aef. 5:22, 23, 25; Aheb. 5:13, 14)

  6. Kodi mungatani kuti muzikwaniritsa chilamulo cha Khristu mukakhala kusukulu? (Sal. 1:1-3; Yoh. 17:14)

  7. Kodi tingatani kuti tizikondana ngati mmene Yesu anatikondera? (Agal. 6:1-5, 10)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena