Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • CO-pgm20 tsamba 2-3
  • Lachisanu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Lachisanu
  • Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2020
  • Nkhani Yofanana
  • Muzisangalatsa Mtima wa Yehova!
    Pulogalamu ya Msonkhano Wadera wa 2020-2021—Wokhala ndi Woyang’anira Dera
  • “Kondwerani Chifukwa cha Zimene Yehova Wachita”
    Pulogalamu ya Msonkhano Wadera wa 2020-2021—Wokhala ndi Woimira Nthambi
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2017
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2019
Onani Zambiri
Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2020
CO-pgm20 tsamba 2-3

Lachisanu

“Nthawi zonse kondwerani mwa Ambuye. Ndibwerezanso, Kondwerani”​—Afilipi 4:4

M’MAWA

  • 9:20 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 9:30 Nyimbo Na. 111 ndi Pemphero

  • 9:40 NKHANI YA TCHEYAMANI: N’chifukwa Chiyani Yehova ndi “Mulungu Wachimwemwe”? (1 Timoteyo 1:11)

  • 10:15 NKHANI YOSIYIRANA: Zimene Zimatithandiza Kukhala Osangalala

    • • Moyo Wosalira Zambiri (Mlaliki 5:12)

    • • Chikumbumtima Chabwino (Salimo 19:8)

    • • Kuona Ntchito Moyenera (Mlaliki 4:6; 1 Akorinto 15:58)

    • • Anzathu Abwino (Miyambo 18:24; 19:4, 6, 7)

  • 11:05 Nyimbo Na. 89 ndi Zilengezo

  • 11:15 KUWERENGA BAIBULO MWASEWERO: “Yehova Anawachititsa Kusangalala” (Ezara 1:1– 6:22; Hagai 1:2-11; 2:3-9; Zekariya 1:12-16; 2:7-9; 3:1, 2; 4:6, 7)

  • 11:45 Tizisangalala ndi Zimene Yehova Amachita Populumutsa Anthu Ake (Salimo 9:14; 34:19; 67:1, 2; Yesaya 12:2)

  • 12:15 Nyimbo Na. 148 ndi Kupuma

MASANA

  • 1:30 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 1:40 Nyimbo Na. 131

  • 1:45 NKHANI YOSIYIRANA: Muzisangalala M’banja Mwanu

    • • Amuna, Muzisangalala ndi Mkazi Wanu (Miyambo 5:18, 19; 1 Petulo 3:7)

    • • Akazi, Muzisangalala ndi Mwamuna Wanu (Miyambo 14:1)

    • • Makolo, Muzisangalala ndi Ana Anu (Miyambo 23:24, 25)

    • • Ananu, Muzisangalala ndi Makolo Anu (Miyambo 23:22)

  • 2:50 Nyimbo Na. 135 ndi Zilengezo

  • 3:00 NKHANI YOSIYIRANA: Chilengedwe Chimasonyeza Kuti Yehova Amafuna Tizisangalala

    • • Maluwa Okongola (Salimo 111:2; Mateyu 6:28-30)

    • • Chakudya Chokoma (Mlaliki 3:12, 13; Mateyu 4:4)

    • • Mitundu Yokongola ya Zinthu (Salimo 94:9)

    • • Thupi Lathu Logometsa (Machitidwe 17:28; Aefeso 4:16)

    • • Kaphokoso Kosangalatsa (Miyambo 20:12; Yesaya 30:21)

    • • Nyama Zochititsa Chidwi (Genesis 1:26)

  • 4:00 Anthu “Olimbikitsa Mtendere Amasangalala” (Miyambo 12:20; Yakobo 3:13-18; 1 Petulo 3:10, 11)

  • 4:20 Kukhala pa Ubwenzi Wolimba ndi Yehova Kumachititsa Kuti Munthu Azisangalala Kwambiri (Salimo 25:14; Habakuku 3:17, 18)

  • 4:55 Nyimbo Na. 28 ndi Pemphero Lomaliza

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena