Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • CO-pgm21 tsamba 2-3
  • Lachisanu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Lachisanu
  • Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2021
  • Nkhani Yofanana
  • Lamlungu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2021
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2021
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2022
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2019
Onani Zambiri
Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2021
CO-pgm21 tsamba 2-3
Zithunzi: 1. Nowa wanyamula nkhwangwa ndipo akuyang’ana mitengo italiitali m’nkhalango. 2. Mlengalenga mukuoneka dziko lapansi, nyenyezi ndi dzuwa. 3. Nangumi ali ndi mwana wake.

Lachisanu

“Tiwonjezereni chikhulupiriro”​—Luka 17:5

M’MAWA

  • 9:20 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 9:30 Nyimbo Na. 5 ndi Pemphero

  • 9:40 NKHANI YA TCHEYAMANI: Kodi Chikhulupiriro Ndi Champhamvu Bwanji? (Mateyu 17:19, 20; Aheberi 11:1)

  • 10:10 NKHANI YOSIYIRANA: N’chifukwa Chiyani Timakhulupirira . . .

    • • Kuti Mulungu Alipo? (Aefeso 2:1, 12; Aheberi 11:3)

    • • Mawu a Mulungu? (Yesaya 46:10)

    • • Mfundo za Makhalidwe Abwino za Mulungu? (Yesaya 48:17)

    • • Kuti Mulungu Amatikonda? (Yohane 6:44)

  • 11:05 Nyimbo Na. 37 ndi Zilengezo

  • 11:15 KUWERENGA BAIBULO MWASEWERO: Nowa Anali Womvera Chifukwa cha Chikhulupiriro (Genesis 6:1–8:22; 9:8-16)

  • 11:45 Muzikhala Ndi Chikhulupiriro Ndipo Musamakayikire (Mateyu 21:21, 22)

  • 12:15 Nyimbo Na. 118 ndi Kupuma

MASANA

  • 1:35 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 1:45 Nyimbo Na. 2

  • 1:50 NKHANI YOSIYIRANA: Muzilimbitsa Chikhulupiriro Chanu Pogwiritsa Ntchito Zinthu za M’chilengedwe

    • • Nyenyezi (Yesaya 40:26)

    • • Nyanja (Salimo 93:4)

    • • Nkhalango (Salimo 37:10, 11, 29)

    • • Mphepo Komanso Madzi (Salimo 147:17, 18)

    • • Zolengedwa za M’madzi (Salimo 104:27, 28)

    • • Matupi Athu (Yesaya 33:24)

  • 2:50 Nyimbo Na. 148 ndi Zilengezo

  • 3:00 Ntchito Zamphamvu za Yehova Zimatichititsa Kukhala Ndi Chikhulupiriro (Yesaya 43:10; Aheberi 11:32-35)

  • 3:20 NKHANI YOSIYIRANA: Muzitsanzira Anthu a Chikhulupiriro, Osati Opanda Chikhulupiriro

    • • Abele, Osati Kaini (Aheberi 11:4)

    • • Inoki, Osati Lameki (Aheberi 11:5)

    • • Nowa, Osati Anthu Ena a M’nthawi Yake (Aheberi 11:7)

    • • Mose, Osati Farao (Aheberi 11:24-26)

    • • Ophunzira a Yesu, Osati Afarisi (Machitidwe 5:29)

  • 4:15 Kodi Mungatani Kuti ‘Mupitirize Kudziyesa Kuti Muone Ngati Mukadali Olimba M’chikhulupiriro’? (2 Akorinto 13:5, 11)

  • 4:50 Nyimbo Na. 119 ndi Pemphero Lomaliza

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena