Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • syr24 tsamba 2
  • Ziwerengero Zonse za 2024

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ziwerengero Zonse za 2024
  • Lipoti la Chaka Chautumiki cha 2024 la Mboni za Yehova Padziko Lonse
  • Nkhani Yofanana
  • Ziwerengero Zonse za 2023
    Lipoti la Chaka cha Utumiki cha 2023 la Mboni za Yehova Padziko Lonse
  • Kodi a Mboni za Yehova Alipo Angati Padziko Lonse?
    Mafunso Ofunsidwa Kawirikawiri
  • Ziwerengero Zonse za 2018
    Lipoti la Chaka cha Utumiki cha 2018 la Mboni za Yehova
  • Ziwerengero Zonse za 2021
    Lipoti la Chaka Chautumiki cha 2021 la Mboni za Yehova Padziko Lonse
Onani Zambiri
Lipoti la Chaka Chautumiki cha 2024 la Mboni za Yehova Padziko Lonse
syr24 tsamba 2

Ziwerengero Zonse za 2024

  • Maofesi a Nthambi a Mboni za Yehova: 84

  • Mayiko Amene Anatumiza Lipoti: 240

  • Mipingo Yonse: 118,767

  • Opezeka pa Chikumbutso Padziko Lonse: 21,119,442

  • Amene Anadya Zizindikiro Padziko Lonse: 23,212

  • Ofalitsa Onse Amene Anagwira Ntchito Yolalikiraa: 9,043,460

  • Avereji ya Ofalitsa Amene Ankalalikira Mwezi Uliwonse: 8,828,124

  • Kuwonjezereka kwa Ofalitsa Kuchokera mu 2023: 2.4

  • Obatizidwa Onseb: 296,267

  • Avereji ya Apainiyac Okhazikika Mwezi Uliwonse: 1,679,026

  • Avereji ya Apainiya Othandiza Mwezi Uliwonse: 867,502

  • Avereji ya Maphunziro a Baibulod Mwezi Uliwonse: 7,480,146

Chaka cha utumiki cha 2024 chinayambira pa 1 September 2023, ndipo chinatha pa 31 August 2024.

a Wofalitsa ndi munthu amene amalalikira mwakhama uthenga wabwino wa Ufumu wa Mulungu. (Mateyu 24:14) Kuti mudziwe mmene timapezera chiwerengerochi, onani nkhani ya pa yakuti, “Kodi a Mboni za Yehova Alipo Angati Padziko Lonse?”

b Kuti mudziwe zimene mungachite kuti mubatizidwe n’kukhala wa Mboni za Yehova, onani nkhani ya pa yakuti, “Kodi Ndingatani Kuti Ndikhale wa Mboni za Yehova?”

c Mpainiya ndi wa Mboni wobatizidwa komanso wachitsanzo chabwino amene amadzipereka kuti azilalikira uthenga wabwino kwa maola enaake mwezi uliwonse.

d Kuti mudziwe zambiri, onani nkhani ya pa yakuti, “Kodi Phunziro la Baibulo Lomwe a Mboni za Yehova Amachititsa Limakhala Lotani?”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena