Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • CO-pgm25 tsamba 2-3
  • Lachisanu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Lachisanu
  • Pulogalamu ya Msonkhano wa 2025
  • Nkhani Yofanana
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2024
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano wa 2025
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2024
  • Lamlungu
    Pulogalamu ya Msonkhano wa 2025
Onani Zambiri
Pulogalamu ya Msonkhano wa 2025
CO-pgm25 tsamba 2-3
Zithunzi: Zimene zili mupulogalamu ya Lachisanu. 1. Yesu akupemphera m’nyumba. 2. Yesu akuyang’ana maufumu adziko lapansi kuchokera pamwamba paphiri. 3. Wachinyamata ali m’chipinda chake ndipo akuganizira mozama.

Lachisanu

“Yehova Mulungu wako ndi amene uyenera kumulambira”​—Mateyu 4:10

M’mawa

  • 8:20 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 8:30 Nyimbo Na. 74 Komanso Pemphero

  • 8:40 NKHANI YA TCHEYAMANI: Kodi Kulambira Koyera Kumatanthauza Chiyani? (Yesaya 48:17; Malaki 3:16)

  • 9:10 VIDIYO:

    Uthenga Wabwino wa Yesu: Gawo 2

    “Uyu ndi Mwana Wanga”​—Mbali Yoyamba (Mateyu 3:1–4:11; Maliko 1:12, 13; Luka 3:1–4:7; Yohane 1:7, 8)

  • 9:40 Nyimbo Na. 122 Komanso Zilengezo

  • 9:50 NKHANI YOSIYIRANA: Kukwaniritsidwa kwa Maulosi Onena za Mesiya​—Mbali Yoyamba

    • • Anavomerezedwa ndi Mulungu (Salimo 2:7; Mateyu 3:16, 17; Machitidwe 13:33, 34)

    • • Anabadwira Mumzere wa Mfumu Davide (2 Samueli 7:12, 13; Mateyu 1:1, 2, 6)

    • • Anadzozedwa Kukhala “Mesiya Mtsogoleri” (Danieli 9:25; Luka 3:1, 2, 21-23)

  • 10:45 Ndi Ndani Kwenikweni Amene Akulamulira Dzikoli? (Maliko 12:17; Luka 4:5-8; Yohane 18:36)

  • 11:15 Nyimbo Na. 22 Komanso Kupuma

Masana

  • 12:35 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 12:45 Nyimbo Na. 121

  • 12:50 NKHANI YOSIYIRANA: Tsanzirani Zimene Yesu Anayankha Pamene Satana Ankamuyesa

    • • Muzichita Zimene Mawu a Yehova Amanena (Mateyu 4:1-4)

    • • Musamamuyese Yehova (Mateyu 4:5-7)

    • • Muzilambira Yehova Yekha (Mateyu 4:10; Luka 4:5-7)

    • • Muziikira Kumbuyo Choonadi (1 Petulo 3:15)

  • 1:50 Nyimbo Na. 97 Komanso Zilengezo

  • 2:00 NKHANI YOSIYIRANA: Zomwe Tikuphunzira pa Moyo wa M’nthawi ya Yesu

    • • Chipululu cha Yudeya (Mateyu 3:1-4; Luka 4:1)

    • • Chigwa cha Yorodano (Mateyu 3:13-15; Yohane 1:27, 30)

    • • Yerusalemu (Mateyu 23:37, 38)

    • • Samariya (Yohane 4:7-9, 40-42)

    • • Galileya (Mateyu 13:54-57)

    • • Foinike (Luka 4:25, 26)

    • • Siriya (Luka 4:27)

  • 3:10 Kodi Yesu Amaona Chiyani mwa Inu? (Yohane 2:25)

  • 3:45 Nyimbo Na. 34 Komanso Pemphero Lomaliza

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena