Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • CO-pgm25 tsamba 6-7
  • Lamlungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Lamlungu
  • Pulogalamu ya Msonkhano wa 2025
  • Nkhani Yofanana
  • Lamlungu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2024
  • Lamlungu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2021
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano wa 2025
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2024
Onani Zambiri
Pulogalamu ya Msonkhano wa 2025
CO-pgm25 tsamba 6-7
Zithunzi: Zimene zili mupulogalamu ya Lamlungu. 1. Mayi wa Chisamariya ali pachitsime. 2. Yesu wanyamula mpukutu wotsekula pamene akulankhula m’sunagoge.

Lamlungu

“Adzalambira Atate motsogoleredwa ndi mzimu ndi choonadi”​—Yohane 4:23

M’mawa

  • 9:20 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 9:30 Nyimbo Na. 140 Komanso Pemphero

  • 9:40 NKHANI YOSIYIRANA: Zimene Tikuphunzira pa Zomwe Yesu Ananena

    • • “Kubadwa mwa Madzi ndi Mzimu” (Yohane 3:3, 5)

    • • “Palibe Munthu Amene Anakwera Kumwamba” (Yohane 3:13)

    • • ‘Fikani Pamene Pali Kuwala’ (Yohane 3:19-21)

    • • “Munthu Ameneyo Ndi Ineyo” (Yohane 4:25, 26)

    • • “Chakudya Changa” (Yohane 4:34)

    • • “M’mindamo . . . Mwayera Kale Ndipo M’mofunika Kukolola” (Yohane 4:35)

  • 11:05 Nyimbo Na. 37 Komanso Zilengezo

  • 11:15 NKHANI YA ONSE: Kodi Zomwe Mumakhulupirira Ndi Zoona? (Yohane 4:20-24)

  • 11:45 Phunziro Lachidule la Nsanja ya Olonda

  • 12:15 Nyimbo Na. 84 Komanso Kupuma

Masana

  • 1:35 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 1:45 Nyimbo Na. 77

  • 1:50 VIDIYO:

    Uthenga Wabwino wa Yesu: Gawo 3

    “Munthu Ameneyo Ndi Ineyo” (Yohane 3:1–4:54; Mateyu 4:12-20; Maliko 1:19, 20; Luka 4:16–5:11)

  • 2:35 Nyimbo Na. 20 Komanso Zilengezo

  • 2:45 Kodi Mwaphunzira Chiyani?

  • 2:55 Pitirizani Kukhala M’kachisi Wamkulu Wauzimu wa Yehova (Aheberi 10:21-25; 13:15, 16; 1 Petulo 1:14-16; 2:21)

  • 3:45 Nyimbo Yatsopano Komanso Pemphero Lomaliza

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena