Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • CO-pgm25 tsamba 4-5
  • Loweruka

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Loweruka
  • Pulogalamu ya Msonkhano wa 2025
  • Nkhani Yofanana
  • Lamlungu
    Pulogalamu ya Msonkhano wa 2025
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2024
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano wa 2025
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2024
Onani Zambiri
Pulogalamu ya Msonkhano wa 2025
CO-pgm25 tsamba 4-5
Zithunzi: Zimene zili mupulogalamu ya Loweruka. 1. Yohane M’batizi wakhala pansi pa mtengo. 2. Yesu akutambasulira dzanja lake munthu wina mosangalala. 3. Azimayi awiri akucheza pa shopu yogulitsira khofi.

Loweruka

“Kudzipereka kwanga panyumba yanu kudzakhala ngati moto umene ukuyaka mumtima mwanga”​—Yohane 2:17

M’mawa

  • 8:20 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 8:30 Nyimbo Na. 93 Komanso Pemphero

  • 8:40 “Kodi Mukufunafuna Chiyani?” (Yohane 1:38)

  • 8:50 VIDIYO:

    Uthenga Wabwino wa Yesu: Gawo 2

    “Uyu ndi Mwana Wanga”​—Mbali Yachiwiri (Yohane 1:19–2:25)

  • 9:20 Nyimbo Na. 54 Komanso Zilengezo

  • 9:30 NKHANI YOSIYIRANA: Muzitsanzira Anthu Amene Ankakonda Kulambira Koyera

    • • Yohane M’batizi (Mateyu 11:7-10)

    • • Andireya (Yohane 1:35-42)

    • • Petulo (Luka 5:4-11)

    • • Yohane (Mateyu 20:20, 21)

    • • Yakobo (Maliko 3:17)

    • • Filipo (Yohane 1:43)

    • • Natanayeli (Yohane 1:45-47)

  • 10:35 NKHANI YA UBATIZO: N’chifukwa Chiyani Mukubatizidwa? (Malaki 3:17; Machitidwe 19:4; 1 Akorinto 10:1, 2)

  • 11:05 Nyimbo Na. 52 Komanso Kupuma

Masana

  • 12:35 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 12:45 Nyimbo Na. 36

  • 12:50 NKHANI YOSIYIRANA: Mmene Tingagwiritsire Ntchito Zomwe Tikuphunzira pa Chozizwitsa Choyambirira cha Yesu

    • • Kusonyeza Chifundo (Agalatiya 6:10; 1 Yohane 3:17)

    • • Kukhala Odzichepetsa (Mateyu 6:2-4; 1 Petulo 5:5)

    • • Kukhala Opatsa (Deuteronomo 15:7, 8; Luka 6:38)

  • 1:20 Kodi “Mwanawankhosa wa Mulungu” Akuchotsa Bwanji Uchimo? (Yohane 1:29; 3:14-16)

  • 1:45 NKHANI YOSIYIRANA: Kukwaniritsidwa kwa Maulosi Onena za Mesiya—Mbali Yachiwiri

    • • Anadzipereka Kwambiri pa Nyumba ya Yehova (Salimo 69:9; Yohane 2:13-17)

    • • Analengeza “Uthenga Wabwino kwa Anthu Ofatsa” (Yesaya 61:1, 2)

    • • Anaonetsa “Kuwala Kwakukulu” ku Galileya (Yesaya 9:1, 2)

  • 2:20 Nyimbo Na. 117 Komanso Zilengezo

  • 2:30 “Chotsani Izi Muno” (Yohane 2:13-16)

  • 3:00 “Ine Ndidzamumanga” (Yohane 2:18-22)

  • 3:35 Nyimbo Na. 75 Komanso Pemphero Lomaliza

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena