Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • CA-brpgm26 tsamba 4
  • Mupeze Mayankho a Mafunso Awa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mupeze Mayankho a Mafunso Awa
  • Pulogalamu ya Msonkhano Wadera Wokhala ndi Woimira Nthambi wa 2025-202
  • Nkhani Yofanana
  • Mupeze Mayankho a Mafunso Awa
    Pulogalamu ya Msonkhano Wadera Wokhala ndi Woyang’anira Dera wa 2025-2026
  • Zosankha Zomwe Zimasonyeza Kuti Timadalira Yehova
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Zimene Inuyo Mwachita
    Kuwerenga Komanso Kuphunzitsa Mwaluso
  • Tizivomereza Modzichepetsa Kuti Sitikudziwa Zonse
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2025
Onani Zambiri
Pulogalamu ya Msonkhano Wadera Wokhala ndi Woimira Nthambi wa 2025-202
CA-brpgm26 tsamba 4

Mupeze Mayankho a Mafunso Awa:

  1. 1. Kodi tingamve bwanji “zimene mzimu ukunena”? (Chiv. 1:3, 10, 11; 3:19)

  2. 2. Kodi n’chiyani chingatithandize kuti tipitirizebe kuchita khama komanso kupirira? (Chiv. 2:4)

  3. 3. Kodi tingakonzekere bwanji kuti tidzathe kupirira molimba mtima tikamadzazunzidwa? (Miy. 29:25; Chiv. 2:10, 11)

  4. 4. Kodi tingatani kuti tisakane kuti timakhulupirira Yesu? (Chiv. 2:12-16)

  5. 5. Kodi tingatani kuti tipitirize kugwira mwamphamvu chimene tili nacho? (Chiv. 2:24, 25; 3:1-3, 7, 8, 10, 11)

  6. 6. Kodi n’chiyani chingatithandize kukhalabe odzipereka? (Chiv. 3:14-19; Mat. 6:25-27, 31-33)

© 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

CA-brpgm26-CN

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena