Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • wp18 No. 1 tsamba 2
  • Mawu Oyamba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mawu Oyamba
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)——2018
  • Nkhani Yofanana
  • Mawu Oyamba
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2017
  • Kodi Malangizo a M’Baibulo ndi Othandizabe Masiku Ano?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)——2018
  • Mawu Oyamba
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2017
  • Kodi a Mboni za Yehova Amakhulupirira Chipangano Chakale?
    Mafunso Ofunsidwa Kawirikawiri
Onani Zambiri
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)——2018
wp18 No. 1 tsamba 2

Mawu Oyamba

KODI BAIBULO NDI LOTHANDIZABE MASIKU ANO?

Popeza masiku ano anthu amagwiritsa ntchito kwambiri intaneti kapena njira zina zamakono pofufuza zimene akufuna, kodi Baibulo ndi lothandizabe kapena mfundo zake n’zachikale? Baibulo limanena kuti:

“Malemba onse anauziridwa ndi Mulungu, ndipo ndi opindulitsa.”​—2 Timoteyo 3:16.

Nsanja ya Olonda iyi ikufotokoza umboni wosonyeza kuti zimene Baibulo limanena kuti lingatithandize pa mbali iliyonse ya moyo wathu ndi zoona.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena