Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/94
  • Mbiri Yateokratiki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mbiri Yateokratiki
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—1994
  • Nkhani Yofanana
  • Mbiri Yateokrase
    Utumiki Wathu wa Ufumu—1996
  • Mbiri Yateokrase
    Utumiki Wathu wa Ufumu—1995
  • Mbiri Yateokrase
    Utumiki Wathu wa Ufumu—1998
Utumiki Wathu wa Ufumu—1994
km 5/94

Mbiri Yateokratiki

Angola: M’mwezi wa December, chiwonkhetso cha magazini ogaŵiridwa chinawonjezeka kuposa pa 10,000, chiŵerengero chapamwamba kuposa chapapitapo. Ofalitsa 21,965 akuchititsa maphunziro a Baibulo 60,691.

Equatorial Guinea: Ofalitsa 219 anasangalala ndi programu yawo ya tsiku la msonkhano wapadera m’December. Panali chiŵerengero chapamwamba cha ofikapo 521 ndipo 7 anabatizidwa.

Guatemala: Ofalitsa 13,243 m’December anakondwera kuona anthu okwanira 32,911 akufika pa Misonkhano yawo Yachigawo ya “Chiphunzitso Chaumulungu.” Panali 597 amene anabatizidwa pamisonkhano imeneyo.

Latvia: Ntchito ikupitabe patsogolo ku Latvia. M’December wapitayo chiŵerengero chapamwamba cha ofalitsa 577 chinachitira lipoti. Maphunziro a Baibulo apanyumba okwanira 1,816 anachititsidwa, ndipo ofalitsa ampingo anagaŵira magazini 20.5 pa avareji.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena