Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 2/00 tsamba 7
  • Yang’anirani Mamvedwe Anu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yang’anirani Mamvedwe Anu
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2000
  • Nkhani Yofanana
  • Khalani Mmvetseri Wabwino
    Buku Lolangiza la Sukulu ya Utumiki Wateokalase
  • Misonkhano Imapindulitsa Achinyamata
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2000
  • “Yang’anirani Mamvedwe Anu”
    Pindulani ndi Sukulu ya Utumiki wa Mulungu
  • Kodi Ndingatani Kuti Ndizimvetsera Mwachidwi?
    Galamukani!—1998
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2000
km 2/00 tsamba 7

Yang’anirani Mamvedwe Anu

Kumvetsera mosamalitsa n’kofunika pamene tili pamisonkhano ya mpingo, yadera, ndi yachigawo. (Luka 8:18) Kodi mungawongolere bwanji luso lanu la kumvetsera?

◼ Peŵani kudya chakudya chambiri nthaŵi ya misonkhano itatsala pang’ono.

◼ Musalole maganizo anu kupita kwina.

◼ Lembani mwachidule mfundo zazikulu.

◼ Ŵerengani malemba amene akuŵerengedwa.

◼ Yankhani ngati papezeka mpata.

◼ Lingalirani nkhani imene ikukambidwayo.

◼ Ganizirani mmene mungagwiritsire ntchito zimene mukumva.

◼ Pambuyo pake, kambiranani zimene mwaphunzira.

Onani Buku Lolangiza la Sukulu ya Utumiki Wateokalase, phunziro 5.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena