Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 5/04 tsamba 3
  • Kugaŵira Buku la Phunzirani kwa Mphunzitsi Waluso

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kugaŵira Buku la Phunzirani kwa Mphunzitsi Waluso
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2004
  • Nkhani Yofanana
  • Zitsanzo za Maulaliki a Utumiki wa Kumunda
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2005
  • Zimene Ana Amafuna Kwa Makolo Awo
    Phunzirani kwa Mphunzitsi Waluso
  • (1) Funso, (2) Lemba, ndi (3) Mutu
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2006
  • Makolo, Tetezani Cholowa Chanu Chamtengo Wapatali
    Nsanja ya Olonda—2005
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2004
km 5/04 tsamba 3

Kugaŵira Buku la Phunzirani kwa Mphunzitsi Waluso

◼ “Kodi mukuganiza kuti dziko likanakhala labwinopo anthu akanakhala kuti amatsatira mawu aŵa? [Ŵerengani Mateyu 7:12a. Ndiyeno yembekezani ayankhe.] Buku ili lili ndi zinthu zambiri zimene tingaphunzire kwa mphunzitsi waluso woposa onse amene anakhalako.” Sonyezani zithunzi ndi mawu ofotokoza zithunzizo pa mutu 17.

◼ “Makolo ambiri masiku ano amayesetsa kuphunzitsa ana awo makhalidwe abwino. Kodi mukuganiza kuti zimenezi n’zofunika? [Yembekezani ayankhe. Ndiyeno ŵerengani Miyambo 22:6.] Onani kuti makolo akulimbikitsidwa kuyamba kuphunzitsa ana awo ali aang’ono. Buku ili lakonzedwa kuti liwathandize kuchita zimenezo.” Sonyezani zithunzi ndi mawu ofotokoza zithunzizo pa mutu 15, 18, kapena 32.

◼ “Nthaŵi zambiri makolo amadabwa ndi mafunso amene ana awo amafunsa. Ena mwa mafunsowo amakhala ovuta kuyankha, si choncho kodi? [Yembekezani ayankhe. Ndiyeno ŵerengani 2 Timoteo 3:14, 15.] Amayi a Timoteo ndi agogo ake akazi anam’phunzitsa zimene Malemba amanena kuyambira ali khanda. Buku ili lingathandize makolo kuchita zomwezo kwa ana awo masiku ano.” Sonyezani zithunzi zingapo ndi mawu ofotokoza zithunzi pa mutu 11 ndi 12 kapena 34 mpaka 36.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena