Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/14 tsamba 1
  • 1914-2014 Patha Zaka 100 Ufumu wa Mulungu Ukulamulira!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • 1914-2014 Patha Zaka 100 Ufumu wa Mulungu Ukulamulira!
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Nkhani Yofanana
  • Patha Zaka 100 Tikulengeza za Ufumu
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • 1922​—Zimene Zinachitika Zaka 100 Zapitazo
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
  • Kodi Ufumu Umene Walamulira kwa Zaka 100 Umakukhudzani Bwanji?
    Nsanja ya Olonda—2014
  • Mwezi wa August Udzakhala Wosaiwalika
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 8/14 tsamba 1

1914-2014 Patha Zaka 100 Ufumu wa Mulungu Ukulamulira!

Mu 1922, M’bale J.F. Rutherford ananena kuti: “Onani, Mfumu yayamba kale kulamulira . . . Lengezani za Mfumu ndi ufumu wake.” Tsopano patha zaka 100 Ufumu wa Mulungu ukulamulira, ndipo mawuwa akupangitsa kuti nafenso masiku ano tizilengeza za Ufumuwu mosangalala. Tiyeni tiyesetse kuthandiza anthu kuti adziwe zokhudza Ufumu wa Mulungu kudzera pa webusaiti yathu. Zimenezi zipangitsa kuti mwezi wa August chaka chino ukhale wosaiwalika.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena