Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 January tsamba 5
  • Yehova Amakwaniritsa Malonjezo Ake

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Amakwaniritsa Malonjezo Ake
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Mmene Mungapezere Malemba M’Baibulo Lanu
    Nkhani Zina
  • Gawo 3 Nthawi Yomwe Zinthu Zinachitika
    Muziyenda Ndi Mulungu Molimba Mtima
  • Mfundo Zazikulu za M’buku la Ezara
    Nsanja ya Olonda—2006
  • Gawo 2 Nthawi Yomwe Zinthu Zinachitika
    Muziyenda Ndi Mulungu Molimba Mtima
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 January tsamba 5

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | EZARA 1-5

Yehova Amakwaniritsa Malonjezo Ake

Losindikizidwa
Aisiraeli anamanganso kachisi ku Yerusalemu

Yehova analonjeza kuti adzabwezeretsa kulambira koona mu Yerusalemu. Koma anthu atamasulidwa ku ukapolo wa ku Babulo, panali mavuto ambiri. Panalinso lamulo loletsa ntchito yomanga malo olambirira moti ambiri ankaganiza kuti ntchitoyo sadzaimaliza.

  1. c. 537 B.C.E.

    Koresi analamula kuti kachisi amangidwenso

  2. 3:3

    Mwezi wa 7

    Guwa linakonzedwa ndipo nsembe zinaperekedwa

  3. 3:10, 11

    536 B.C.E.

    Maziko anamangidwa

  4. 4:23, 24

    522 B.C.E.

    Mfumu Aritasasita inaimitsa ntchito yomanga

  5. 5:1, 2

    520 B.C.E.

    Zekariya ndi Hagai analimbikitsa anthu kuti ayambirenso kumanga

  6. 6:15

    515 B.C.E.

    Ntchito yomanga kachisi inamalizidwa

    Mabuku a Chichewa (1974-2026)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena