Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 February tsamba 3
  • Nehemiya Anali Woyang’anira Wabwino

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nehemiya Anali Woyang’anira Wabwino
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Mfundo Zazikulu za M’buku la Nehemiya
    Nsanja ya Olonda—2006
  • “Pitirizani Kugonjetsa Choipa mwa Kuchita Chabwino”
    Nsanja ya Olonda—2007
  • “Inu Mulungu Wanga, Mundikumbukire pa Zabwino Zimene Ndinachita”
    Nsanja ya Olonda—2011
  • Nehemiya Ankakonda Kulambira Yehova
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 February tsamba 3

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | NEHEMIYA 5-8

Nehemiya Anali Woyang’anira Wabwino

Tishiri 455 B.C.E.

8:1-18

  1. N’kutheka kuti panthawiyi m’pamene Nehemiya anasonkhanitsa anthu kuti alambire Yehova

  2. Anthu anasangalala kwambiri

  3. Anthu amene anali mitu ya mabanja anasonkhana kuti aone zimene angachite kuti azitsatira kwambiri Chilamulo cha Mulungu

  4. Anthu anakonzekera kuchita Chikondwerero cha Misasa

Mwezi wa Tishiri 455 B.C.E. Aisiraeli anasonkhana kuti alambire Mulungu, alandire malangizo komanso achite Chikondwerero cha Misasa.
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena