Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 June tsamba 4
  • Yehova Amasamalira Anthu Omwe Akudwala

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Amasamalira Anthu Omwe Akudwala
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • “Ndiphunzitseni Kuchita Chifuniro Chanu”
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Yehova ‘Anapulumutsa’ Anthu Ake M’nthawi za M’baibulo
    Nsanja ya Olonda—2008
  • Dalirani Mzimu wa Mulungu Zinthu Zikasintha pa Moyo Wanu
    Nsanja ya Olonda—2004
  • Tizidalira Yehova Kuti Tikhale Olimba Mtima
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 June tsamba 4

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MASALIMO 38-44

Yehova Amasamalira Anthu Omwe Akudwala

Anthu amene amatumikira Yehova mokhulupirika amamudalira pa mavuto aliwonse

Davide akudwala ndipo wagona pabedi

41:1-4

  • Davide anadwala kwambiri

  • Davide ankathandiza anthu onyozeka

  • Davide sankayembekezera kuti achira mozizwitsa, koma anapempha Yehova kuti amupatse nzeru, amutonthoze ndiponso amuthandize

  • Yehova ankaona kuti Davide anali munthu wokhulupirika

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena