Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 July tsamba 8
  • Ndandanda ya Upainiya Wokhazikika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Upainiya Wokhazikika
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Ndandanda za Upainiya Wothandiza
    Utumiki Wathu wa Ufumu—1997
  • Kodi Tsopano Khomo Lochita Upainiya Lakutsegukirani?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—1999
  • Nyengo ya Chikumbutso ndi Nthawi Yochita Zambiri
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2005
  • Utumiki Waupainiya—Kodi Ngoyenera Inu?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—1998
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 July tsamba 8

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Ndandanda ya Upainiya Wokhazikika

Apainiya awiri akulalikira munthu

Kuti munthu akwanitse kuchita upainiya wokhazikika amafunika kugawa bwino nthawi yake. Ngati mutamalalikira maola 18 pa mlungu, ndiye kuti mukhoza kupeza nthawi ina yochita zinthu zina komanso kupuma. Kuwonjezera pamenepa, simungavutike kukwanitsa maola ngati mutadwala mwadzidzidzi kapena ngati nyengo sili bwino. Ndandanda imene ili m’munsiyi ingakuthandizeni kugawa bwino nthawi yanu ngati mumagwira ntchito yaganyu, ntchito yolembedwa kapena ngati mumadwaladwala. Komanso ngati mutasintha zina ndi zina m’banja lanu, munthu mmodzi kapena angapo akhoza kuyamba upainiya mwezi wa September. Bwanji osakambirana zimenezi pa kulambira kwanu kwa pabanja kwa mlungu wotsatira?

NDIMAGWIRA NTCHITO YAGANYU

Lolemba

NTCHITO

Lachiwiri

NTCHITO

Lachitatu

NTCHITO

Lachinayi

Maola 6

Lachisanu

Maola 6

Loweruka

Maola 4

Lamlungu

Maola 2

NDIMAGWIRA NTCHITO YOLEMBEDWA

Lolemba

Maola Awiri

Lachiwiri

Maola Awiri

Lachitatu

MISONKHANO YA MKATI MWA MLUNGU

Lachinayi

Maola Awiri

Lachisanu

Maola Awiri

Loweruka

Maola 6

Lamlungu

Maola 4

NDIMADWALADWALA

Lolemba

KUPUMA

Lachiwiri

Maola 3

Lachitatu

Maola 3

Lachinayi

Maola 3

Lachisanu

Maola 3

Loweruka

Maola 3

Lamlungu

Maola 3

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena