Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 August tsamba 6
  • ‘Muziyamikira Yehova’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Muziyamikira Yehova’
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Yamikani Yehova Ndipo Adzakudalitsani
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Kodi Mukuyang’ana pa Mphoto?
    Nsanja ya Olonda—2004
  • Lemba la Chaka cha 2015
    Buku Lapachaka la Mboni za Yehova la 2015
  • Pemphero Lothokoza
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 August tsamba 6

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MASALIMO 106-109

‘Muziyamikira Yehova’

Mose ndi Aisiraeli akuyamikira Yehova

N’chifukwa chiyani Aisiraeli anaiwala mwamsanga zimene Yehova anawachitira?

106:7, 13, 14

  • Anasiya kuganizira za Yehova n’kuyamba kuganizira mavuto komanso zofuna zawo

Kodi tingatani kuti tizithokoza Yehova komanso kuti tisamaiwale zomwe watichitira?

106:1-5

  • Tiziganizira zinthu zonse zimene Yehova watichitira

  • Tiziganizira zimene Mulungu walonjeza kudzatichitira m’tsogolo

  • Tizithokoza Yehova tikaona kuti watichitira zomwe tinapempha

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena