Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 November tsamba 8
  • Msulami Ndi Chitsanzo Chabwino Kwambiri kwa Atumiki a Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Msulami Ndi Chitsanzo Chabwino Kwambiri kwa Atumiki a Yehova
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Chitsanzo Chabwino—Msulami
    Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Lachiwiri
  • Mfundo Zazikulu za Nyimbo ya Solomo
    Nsanja ya Olonda—2006
  • Chikondi Chowona Chiri Chachipambano!
    Nsanja ya Olonda—1987
  • Kodi N’zotheka Kukondana Mpaka Kalekale?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 November tsamba 8

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | NYIMBO YA SOLOMO 1-8

Msulami Ndi Chitsanzo Chabwino Kwambiri kwa Atumiki a Yehova

N’chifukwa chiyani tinganene kuti mtsikanayu ndi chitsanzo chabwino?

2:7; 4:12

Msulami ali ndi atsikana ena a ku Yerusalemu
  • Anali wanzeru ndipo anadikira mpaka atapeza chikondi chenicheni

  • Sankalola kuti anthu ena amukakamize kuti ayambe chibwenzi ndi munthu wina aliyense

  • Anali wodzichepetsa, wosakonda chuma komanso wodzisunga

  • Sanakopeke ndi zinthu ngati golide kapena mawu okopa achikondi

Dzifunseni kuti:

‘Kodi ndi khalidwe liti la mtsikanayu limene ndiyenera kuyesetsa kumutsanzira?’

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena