Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 April tsamba 1
  • Zitsanzo za Ulaliki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zitsanzo za Ulaliki
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • GALAMUKANI!
  • KUPHUNZITSA CHOONADI
  • KODI UFUMU WA MULUNGU N’CHIYANI? (Ulendo wobwereza)
  • LEMBANI ULALIKI WANUWANU
  • Mawu Oyamba
    Galamukani!—2017
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 April tsamba 1
Mlongo amene anafooka walandiridwa ndi manja awiri kumpingo

Mlongo amene anafooka walandiridwanso kumpingo

Zitsanzo za Ulaliki

GALAMUKANI!

Galamukani! Na. 2 2017 | Kodi Ndi Bwino Kukhulupirira Zamatsenga?

Funso: Masiku ano, mafilimu ndi mapulogalamu a pa TV amakonda kuonetsa zamatsenga monga zokhudza ufiti, mizukwa ndi zina. Kodi mumaona kuti pali vuto lililonse kuonera zinthu zimenezi?

Perekani Magaziniyo: Galamukani! iyi ikufotokoza chifukwa chimene anthu ena amachitira chidwi ndi nkhani zamatsenga komanso zoona zake za nkhaniyi.

KUPHUNZITSA CHOONADI

Baibulo lotsegula

Funso: Kodi Ufumu wa Mulungu udzathetsa bwanji mavuto padzikoli?

Lemba: Mat. 6:10

Zoona Zake: Ufumu wa Mulungu udzabweretsa mtendere, mgwirizano komanso chitetezo padzikoli ngati mmene zilili kumwamba.

KODI UFUMU WA MULUNGU N’CHIYANI? (Ulendo wobwereza)

Kodi Ufumu wa Mulungu N’chiyani?

Funso: [Musonyezeni funso limene mudzakambirane pa ulendo wotsatira lomwe lili kuseri kwa kapepalaka.] Kodi moyo udzakhala wotani mu Ufumu wa Mulungu?

Malemba: Sal. 37:29; Yes. 65:21-23

Perekani Kabuku: [Musonyezeni kabuku ka Uthenga Wabwino.] Phunziro 7 m’kabukuka likufotokoza mmene anthufe tidzapindulire malonjezo amenewa akadzakwaniritsidwa. [Yambitsani phunziro la Baibulo pogwiritsa ntchito kabukuka.]

LEMBANI ULALIKI WANUWANU

Potengera zitsanzozi, konzani njira imene mungagwiritse ntchito.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena