Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 February tsamba 1
  • Zitsanzo za Ulaliki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zitsanzo za Ulaliki
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • GALAMUKANI!
  • GALAMUKANI!
  • MVERANI MULUNGU
  • LEMBANI NJIRA INA IMENE MUNGAGWIRITSE NTCHITO
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 February tsamba 1
Akulalikira ku Indonesia pogwiritsa ntchito kabuku kakuti Mverani Mulungu

Alongo a ku Indonesia akulalikira pogwiritsa ntchito kabuku kakuti Mverani Mulungu

Zitsanzo za Ulaliki

GALAMUKANI!

Magazini ya Galamukani! Na. 1 2016 | N’zotheka Kumasangalalabe Ngakhale Muli Ndi Mavuto

Funso: Ndabwera kudzakupatsani magazini yatsopano ya Galamukani! Ndikufuna ndimve maganizo anu pa funso ili lomwe lili patsamba 2.

Lemba: Miy. 24:10

Perekani Magaziniyo: Nkhani imeneyi ikufotokoza mfundo zinanso zothandiza.

GALAMUKANI!

Funso: Anthu ambiri amaona kuti n’zothandiza kusankha bwino anzawo apamtima. Kodi inunso mumaona choncho?

Lemba: Miy. 13:20

Perekani Magaziniyo: Magazini iyi ili ndi mfundo zimene zingatithandize kupeza anzathu abwino apamtima. [Musonyezeni nkhani imene ili patsamba 10 ndi 11.]

MVERANI MULUNGU

Listen to God brochure

Funso: Kodi mungakonde kudzakhala m’dziko looneka chonchi? [Musonyezeni tsamba 2 ndi 3, kenako yembekezani kuti ayankhe.]

Lemba: Yer. 29:11

Perekani Kabukuko: Kabuku aka kakufotokoza zimene tingachite kuti tizimvera Mulungu n’kudzalandira madalitso amene watikonzera. [Kambiranani zimene zili patsamba 4 ndi 5.]

LEMBANI NJIRA INA IMENE MUNGAGWIRITSE NTCHITO

Potengera zitsanzozi, konzani njira imene mungagwiritse ntchito.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena