Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 January tsamba 1
  • Zitsanzo za Ulaliki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zitsanzo za Ulaliki
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • NSANJA YA OLONDA
  • NSANJA YA OLONDA (tsamba lomaliza)
  • UTHENGA WABWINO WOCHOKERA KWA MULUNGU!
  • LEMBANI NJIRA INA IMENE MUNGAGWIRITSE NTCHITO
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 January tsamba 1
Alongo akugwiritsa ntchito kabuku kakuti Uthenga Wabwino ku Madagascar

Alongo akugwiritsa ntchito kabuku kakuti Uthenga Wabwino ku Madagascar

Zitsanzo za Ulaliki

NSANJA YA OLONDA

Tsamba loyamba la Nsanja ya Olonda, Na. 1 2016 | N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kuchita Zinthu Moona Mtima?

Funso: Kodi aliyense akanakhala kuti amatsatira mfundo iyi, bwenzi zinthu zili bwanji m’dzikoli?

Lemba: Aheb. 13:18

Perekani Magaziniyo: Baibulo limatilimbikitsa kuti tizikhala oona mtima pa zonse zimene timachita. Nsanja ya Olonda iyi ikufotokoza nkhani imeneyi.

NSANJA YA OLONDA (tsamba lomaliza)

Funso: Ndikufuna ndimve maganizo anu pa funso ili. [Werengani Funso loyamba.] Anthu ena amakhulupirira kuti akamwalira, chinachake chimakhalabe ndi moyo, koma ena amati imfa ndi mapeto a zonse. Kodi inuyo mumakhulupirira chiyani?

Lemba: Mlal. 9:5

Perekani Magaziniyo: Mutu uwu ukufotokoza zimene Baibulo limanena pankhaniyi. Ndikusiyirani kuti muwerenge kenako tidzakambirane paulendo wotsatira.

UTHENGA WABWINO WOCHOKERA KWA MULUNGU!

Tsamba loyamba la kabuku kakuti Uthenga Wabwino Wochokera kwa Mulungu

Perekani Kabukuko: Ndimati ndikupempheni kuti ndiziphunzira nanu Baibulo kwaulere. Kabuku aka kangakuthandizeni kupeza mayankho a mafunso ofunika kwambiri m’Baibulo.

Funso: Kodi inuyo munawerengapo Baibulo? Kuphunzira kwake n’kosavuta. Bwanji ndikusonyezeni? [Kambiranani funso loyamba la Phunziro 2.]

Lemba: Chiv. 4:11

LEMBANI NJIRA INA IMENE MUNGAGWIRITSE NTCHITO

Potengera zitsanzozi, konzani njira imene mungagwiritse ntchito.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena