Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 January tsamba 1
  • Zitsanzo za Ulaliki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zitsanzo za Ulaliki
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • NSANJA YA OLONDA
  • KUPHUNZITSA CHOONADI
  • KODI MUKUFUNA KUDZIWA CHOONADI?
  • LEMBANI ULALIKI WANUWANU
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 January tsamba 1
A Mboni za Yehova akulalikira uthenga wabwino ku Ghana

Ntchito yolalikira uthenga wabwino ku Ghana

Zitsanzo za Ulaliki

NSANJA YA OLONDA

Nsanja ya Olonda Na. 1 2017 | Kodi Mungatani Kuti Kuwerenga Baibulo Kuzikusangalatsani?

Funso: Anthu ena amaganiza kuti Baibulo ndi lachikale, pomwe ena amaona kuti ndi lothandizabe. Kodi inuyo mukuganiza bwanji?

Lemba: 2 Tim. 3:16, 17

Perekani Magaziniyo: Nsanja ya Olonda iyi ikusonyeza kuti m’Baibulo muli malangizo anzeru komanso ikufotokoza zimene mungachite kuti muzipindula kwambiri mukamawerenga Baibulo.

KUPHUNZITSA CHOONADI

Baibulo lotsegula

Funso: Kodi n’zoona kuti mapeto a dzikoli ali pafupi?

Lemba: Mat. 24:3, 7, 14

Zoona Zake: Ulosi wa m’Baibulo umasonyeza kuti tikukhala m’masiku otsiriza. Mfundoyi ndi yosangalatsa chifukwa ikusonyeza kuti mavuto athu atsala pang’ono kutha.

KODI MUKUFUNA KUDZIWA CHOONADI?

Kodi Mukufuna Kudziwa Choonadi?

Funso: Kodi Mulungu amatiganiziradi?

Lemba: 1 Pet. 5:6, 7

Perekani Kapepalako: Kapepalaka kali ndi malemba ena amene akuyankha funsoli komanso kali ndi mayankho a mafunso ena 5 ofunika kwambiri.

LEMBANI ULALIKI WANUWANU

Potengera zitsanzozi, konzani njira imene mungagwiritse ntchito.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena