Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 June tsamba 1
  • Zitsanzo za Ulaliki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zitsanzo za Ulaliki
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • GALAMUKANI!
  • GALAMUKANI!
  • TIMAPEPALA
  • LEMBANI NJIRA INA IMENE MUNGAGWIRITSE NTCHITO
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 June tsamba 1
Ofalitsa akulalikira pogwiritsa ntchito kapepala ku Malta

Ofalitsa akulalikira pogwiritsa ntchito kapepala ku Malta

Zitsanzo za Ulaliki

GALAMUKANI!

Galamukani! Na. 3 2016 | A Mboni za Yehova Akumasulira M’zinenero Zambiri

Perekani Magaziniyo: Galamukani! iyi ikufotokoza nkhani yochititsa chidwi. [Mpatseni magaziniyo.]

Funso: Kodi mukudziwa kuti a Mboni za Yehova amamasulira mabuku m’zinenero zoposa 750?

Lemba: Chiv. 14:6

GALAMUKANI!

Funso: Kodi mukuona kuti mfundo iyi ingathandize anthu okwatirana pamene akukambirana vuto linalake?

Lemba: Yak. 1:19

Perekani magaziniyo: [Musonyezeni nkhani yomwe yayambira patsamba 10.] Nkhaniyi ikufotokoza mfundo zinanso za m’Baibulo zomwe zingathandize anthu okwatirana.

TIMAPEPALA

Kapepala

Funso: Taonani funso ili. [Werengani funso lomwe lili pakapepalako losonyeza mayankho angapo.] Inuyo mukuganiza bwanji?

Lemba: [Lili patsamba 2 la kapepalako]

Perekani Kapepalako: Kapepalaka kakufotokoza zimene mungaphunzire palembali.

LEMBANI NJIRA INA IMENE MUNGAGWIRITSE NTCHITO

Potengera zitsanzozi, konzani njira imene mungagwiritse ntchito.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena