Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 April tsamba 7
  • Khalani Olimba Mtima Ngati Yeremiya

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Khalani Olimba Mtima Ngati Yeremiya
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Yeremiya—Mneneri Wachilendo wa Ziweruzo za Mulungu
    Nsanja ya Olonda—1988
  • “Ndaika Mawu Anga M’kamwa Mwako”
    Zimene Mulungu Akutiuza Kudzera mwa Yeremiya
  • Yehova Anauza Yeremiya Kuti Azilalikira
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Kodi Mumasankha Anthu Otani Kuti Akhale Anzanu?
    Zimene Mulungu Akutiuza Kudzera mwa Yeremiya
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 April tsamba 7

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YEREMIYA 25-28

Khalani Olimba Mtima Ngati Yeremiya

Mneneri Yeremiya akuchenjeza kuti Yerusalemu awonongedwa

Yeremiya anachenjeza kuti Yerusalemu adzawonongedwa ngati mmene anawonongedwera Silo

26:6

  • Pa nthawi ina, likasa la pangano lomwe linali umboni woti Yehova ankatsogolera anthu ake, linkasungidwa ku Silo

  • Yehova analola kuti Afilisiti akalande likasalo ndipo silinabwererenso ku Silo

Ansembe, aneneri, ndiponso anthu agwira mneneri Yeremiya

Ansembe, aneneri ndi anthu onse ankafuna kupha Yeremiya

26:8, 9, 12, 13

  • Anthu anagwira Yeremiya chifukwa ankanena za kuwonongedwa kwa Yerusalemu ndi kachisi

  • Yeremiya sanathawe kapena kusiya kutumikira Mulungu

Mneneri Yeremiya

Yehova anateteza Yeremiya

26:16, 24

  • Yeremiya anapitiriza kukhala wolimba mtima ndipo Yehova sanamusiye

  • Mulungu anachititsa kuti Ahikamu, yemwe anali wolimba mtima, ateteze Yeremiya

Yeremiya analengeza uthenga kwa zaka 40 ngakhale kuti anthu ambiri sankasangalala nawo. Iye anakwanitsa zimenezi chifukwa choti yehova ankamulimbikitsa komanso kumuthandiza

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena