CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | EZEKIELI 24-27
Ulosi Wonena za Kuwonongedwa kwa Turo Umatithandiza Kuti Tizikhulupirira Kwambiri Mawu a Yehova
Losindikizidwa
Buku la Ezekieli linaneneratu mwatsatanetsatane za mmene mzinda wa Turo udzawonongedwere.
Kodi ndani anawononga mzinda wa Turo patapita nthawi kuchokera mu 607 B.C.E.?
Kodi ndani anatenga dothi ndi zogumuka za mabwinja a mzinda wa Turo M’chaka cha 332 B.C.E., n’kukazithira m’nyanja kuti apange njira pokawononga mbali ina ya mzindawo yomwe inali panyanja?