Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 October tsamba 4
  • Yehova Ananeneratu Zokhudza Mafumu a Mtsogolo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Ananeneratu Zokhudza Mafumu a Mtsogolo
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Grisi—Mphamvu Yaikulu ya Dziko Yachisanu
    Nsanja ya Olonda—1988
  • Mafumu Aŵiri Olimbana
    Samalani Ulosi wa Danieli!
  • Ndani Adzalamulira Dziko?
    Samalani Ulosi wa Danieli!
  • Buku Limene Mungathe Kulikhulupirira—Gawo 5
    Galamukani!—2011
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 October tsamba 4

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | DANIELI 10-12

Yehova Ananeneratu Zokhudza Mafumu a Mtsogolo

11:2

Padzakhala mafumu 4 ochokera mu ufumu wa Perisiya. Mfumu ya nambala 4 “idzaukira ufumu wa Girisi ndi mphamvu zake zonse.”

  1. Koresi Wamkulu

  2. Kambisesi II

  3. Dariyo I

  4. Sasta I (ena amati ndi Mfumu Ahasiwero amene anakwatira Esitere)

11:3

Mfumu yamphamvu ya Girisi inayamba kulamulira dera lalikulu kwambiri.

  • Alekizanda Wamkulu

11:4

Akuluakulu 4 a asilikali a Alekizanda anagawana ufumu wa Girisi.

  1. Kasanda

  2. Lasamekasi

  3. Selukasi I

  4. Tolemi I

Akuluakulu 4 a asilikali a Alekizanda anagawana ufumu wa Girisi
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena