Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 December tsamba 6
  • Kodi Ukwati Wanu Umakondweretsa Yehova?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Ukwati Wanu Umakondweretsa Yehova?
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Nkusudzula kwa Mtundu Wotani Kumene Mulungu Amada?
    Galamukani!—1994
  • Yehova Amadana ndi Chinyengo
    Nsanja ya Olonda—2002
  • Yesetsani Kuti Banja Lanu Lizikondweretsa Mulungu
    Muzikumbukira Tsiku la Yehova Nthawi Zonse
  • Pambuyo pa Tsiku la Ukwati
    Kodi Mungatani Kuti Mulungu Azikukondani?
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 December tsamba 6
Bambo wachiisiraeli akusiya mkazi wake

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MALAKI 1-4

Kodi Ukwati Wanu Umakondweretsa Yehova?

2:13-16

  • M’nthawi ya Malaki, anthu ambiri ankathetsa ukwati pa zifukwa zosamveka. Yehova sankavomereza kulambira kwa munthu amene wachitira zachinyengo mwamuna kapena mkazi wake

  • Yehova anadalitsa anthu amene ankalemekeza amuna kapena akazi awo

Kodi anthu okwatirana angasonyeze bwanji kuti ndi okhulupirika kwa mnzawo pa zimene . . .

  • amaganiza?

  • amayang’ana kapena kuonera?

  • amalankhula?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena