Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 March tsamba 1
  • Zimene Tinganene

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Tinganene
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • ●○○ ULENDO WOYAMBA
  • ○●○ ULENDO WOBWEREZA WOYAMBA
  • ○○● ULENDO WOBWEREZA WACHIWIRI
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Zimene Tinganene
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 March tsamba 1
Akuitanira anthu ku Chikumbutso

Akuitanira anthu ku Chikumbutso ku Slovenia

Zimene Tinganene

●○○ ULENDO WOYAMBA

Ntchito Yogawira Kapepala Koitanira Anthu ku Chikumbutso (March 3-31): Tikukuitanani ku mwambo wofunika kwambiri. Kapepala kanu ndi kameneka. Loweruka pa 31 March, anthu mamiliyoni ambiri padziko lonse adzasonkhana kuti achite mwambo wokumbukira imfa ya Yesu Khristu. Kapepalaka kakusonyeza nthawi komanso malo omwe mwambowu udzachitikire m’dera lathu lino. Tikukuitananinso kuti mudzamvetsere nkhani ya mutu wakuti, “Kodi Yesu Khristu Ndi Ndani Kwenikweni?” yomwe idzakambidwe kutatsala mlungu umodzi kuti mwambowu uchitike.

Funso la Ulendo Wotsatira Ngati Wasonyeza Chidwi: N’chifukwa chiyani Yesu anafa?

○●○ ULENDO WOBWEREZA WOYAMBA

Funso: N’chifukwa chiyani Yesu anafa?

Lemba: Mat. 20:28

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi dipo la Yesu lingatithandize bwanji?

○○● ULENDO WOBWEREZA WACHIWIRI

Funso: Kodi dipo la Yesu lingatithandize bwanji?

Lemba: Aroma 6:23

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi tingasonyeze bwanji kuti timayamikira dipo?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena