Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 April tsamba 3
  • Kodi Tingamvere Bwanji Lamulo Lakuti, Pitani Mukaphunzitse Anthu?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Tingamvere Bwanji Lamulo Lakuti, Pitani Mukaphunzitse Anthu?
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • ‘Aphunzitseni Kusunga Zinthu Zonse Zimene Ndinakulamulirani’
    Nsanja ya Olonda—2004
  • Muzithandiza Ena Kuti Azimvera Malamulo a Khristu
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2020
  • Phunzitsani Anthu Ofatsa Kuyenda M’njira ya Mulungu
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2006
  • “Pitani Mukaphunzitse Anthu . . . Kuti Akhale Ophunzira Anga”
    ‘Bwera Ukhale Wotsatira Wanga’
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 April tsamba 3
Yesu analamula otsatira ake kuti aziphunzitsa anthu

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MATEYU 27-28

Kodi Tingamvere Bwanji Lamulo Lakuti, Pitani Mukaphunzitse Anthu?

28:18-20

N’chifukwa chiyani tiyenera kulalikira? Yesu anapatsidwa ulamuliro waukulu ndi Yehova

Kodi tiyenera kukalalikira kuti? Yesu analamula otsatira ake kuti akaphunzitse “anthu a mitundu yonse”

Kuphunzitsa ena kuti azisunga zinthu zonse zimene Yesu analamula sikumatha

  • Akuphunzira Baibulo ndi munthu

    Kodi tingaphunzitse bwanji ena zimene Yesu analamula?

  • Kuthandiza wophunzira kuti azigwiritsa ntchito zimene Yesu anaphunzitsa

    Kodi tingathandize bwanji wophunzira wathu kuti azigwiritsa ntchito zimene Yesu anaphunzitsa?

  • Kupita limodzi ndi wophunzira mu utumiki

    Kodi tingathandize bwanji wophunzira wathu kuti azitengera chitsanzo cha Yesu?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena