Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 August tsamba 5
  • “Chipulumutso Chanu Chikuyandikira”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Chipulumutso Chanu Chikuyandikira”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Limbani Mtima pamene Chilanditso Chikuyandikira
    Nsanja ya Olonda—1997
  • Muzisonyeza Kuti Mumaona Moyo Mmene Yehova Amauonera
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • “Mupitirize Kukonda Abale”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
  • Kodi Mumayamikira Zimene Yehova Wachita Kuti Akupulumutseni?
    Nsanja ya Olonda—2009
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 August tsamba 5

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | LUKA 21-22

“Chipulumutso Chanu Chikuyandikira”

Yesu wakwera hatchi yoyera

21:25-28

Posachedwapa Yesu abwera kudzawononga oipa ndi kupulumutsa anthu okhulupirika. Tiyenera kukhala okonzeka kuti tidzapulumuke.

KODI TINGAKONZEKERE BWANJI?

  • Tiyenera KUMADALIRA KWAMBIRI YEHOVA,

  • kuti tizichita zinthu MOLIMBA MTIMA,

  • zomwe zimatithandiza kuti TIZIONA ZINTHU MOYENERA,

  • ndipo zimenezi, limodzi ndi KUKONDA ABALE NDI ALONGO ATHU,

  • zingachititse kuti TIZIWALIMBIKITSA

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena