Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 August tsamba 8
  • Muzisonyeza Kuti Mumaona Moyo Mmene Yehova Amauonera

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzisonyeza Kuti Mumaona Moyo Mmene Yehova Amauonera
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • “Chipulumutso Chanu Chikuyandikira”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • ‘Mulungu Anayesa Abulahamu’
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Muzilemekeza Anthu Ena
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2025
  • Zochita Zanu Zingathandize Banja Lanu Kukhala Losangalala
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 August tsamba 8
Zithunzi: 1. M’bale wachinyamata wanyamulira mayi wachikulire zinthu zimene wagula ndipo akukwera nazo pamasitepe. 2. Mlongo akulalikira kwa mzimayi pam’jigo.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | EKISODO 21-22

Muzisonyeza Kuti Mumaona Moyo Mmene Yehova Amauonera

21:20, 22, 23, 28, 29

Yehova amaona kuti moyo ndi wamtengo wapatali. Kodi tingasonyeze bwanji kuti nafenso timaona moyo mofananamo?

  • Tizikonda komanso kulemekeza kwambiri anthu ena.—Mt 22:39; 1Yo 3:15

  • Tizionetsa kuti tili ndi chikondi choterocho pochita khama kwambiri mu utumiki.​—1Ak 9:22, 23; 2Pe 3:9

  • Nthawi zonse tiziganizira zimene tingachite kuti tipewe ngozi.​—Miy 22:3

Kodi kuona kuti moyo ndi wamtengo wapatali kumatithandiza bwanji kuti tisakhale ndi mlandu wamagazi?

M’bale akuyasamula pamene akuyendetsa galimoto usiku kwambiri.
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena