Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 September tsamba 2
  • Chozizwitsa Choyamba cha Yesu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chozizwitsa Choyamba cha Yesu
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • “Khalani Oyera”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Yehova Analenga Zamoyo Padziko Lapansi
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • “Machimo Ako Akhululukidwa”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Zozizwitsa Zimene Zichitike Posachedwapa
    Nsanja ya Olonda—2012
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 September tsamba 2

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YOHANE 1-2

Chozizwitsa Choyamba cha Yesu

2:1-11

Chozizwitsa choyamba chimene Yesu anachita chimatithandiza kumudziwa bwino. Kodi mavesiwa akusonyeza bwanji kuti Yesu anali ndi makhalidwe otsatirawa?

  • Ankaona moyenera zosangalatsa komanso ankapeza nthawi yocheza ndi anzake

  • Ankaganizira mmene anthu ena akumvera

  • Anali wowolowa manja

Yesu akuuza munthu kuti adzadzitse mitsuko ndi madzi, woyang’anira phwando akulawa vinyo, kenako akuyamikira mkwati chifukwa cha vinyo wokomayo
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena