Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 November tsamba 2
  • “Kodi Umandikonda Ine Kuposa Izi?”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Kodi Umandikonda Ine Kuposa Izi?”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Muzikhala ndi Makhalidwe Abwino
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Yehova Amakwaniritsa Zomwe Walonjeza
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Mafunso Ochokera kwa Oŵerenga
    Nsanja ya Olonda—1988
  • Kupereka Mnzako kwa Mdani N’koipa Kwambiri
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 November tsamba 2
Ophunzira a Yesu akukokera kumtunda ukonde wodzadza ndi nsomba

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YOHANE 20-21

“Kodi Umandikonda Ine Kuposa Izi?”

21:1-19

Asodzi aluso ankakhala oleza mtima, akhama komanso ankapirira mavuto osiyanasiyana n’cholinga choti aphe nsomba zambiri. (w12 8/1 18-20) Makhalidwe amenewa akanathandiza Petulo monga msodzi wa anthu. Komabe Petulo ankafunika kusankha chinthu choti aike pamalo oyamba m’moyo wake. Ankafunika kusankha ntchito yausodzi yomwe ankaikonda kwambiri kapena kudyetsa otsatira a Yesu mwauzimu.

Kodi mwasintha zinthu zotani pa moyo wanu kuti muziika zinthu zokhudza Ufumu pamalo oyamba?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena