Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 November tsamba 3
  • Mpingo Wachikhristu Unalandira Mzimu Woyera

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mpingo Wachikhristu Unalandira Mzimu Woyera
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • “Anadzazidwa ndi Mzimu Woyera”
    ‘Kuchitira Umboni Mokwanira za Ufumu wa Mulungu’
  • Anaimbidwa Mlandu Wosokoneza Anthu Komanso Kuukira Boma
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Paulo Anapempha Kukaonekera kwa Kaisara Ndipo Kenako Analalikira Mfumu Herode Agiripa
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 November tsamba 3

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MACHITIDWE 1-3

Mpingo Wachikhristu Unalandira Mzimu Woyera

Anthu olankhula zinenero zosiyanasiyana ali ku Yerusalemu pa Pentekosite mu 33 C.E.

2:1-8, 14, 37, 38, 41-47

Ayuda ambiri omwe anapita ku Yerusalemu pa Pentekosite mu 33 C.E. anali oti achokera m’mayiko ena. (Mac. 2:9-11) Ngakhale kuti ankatsatira Chilamulo cha Mose, Ayuda amenewa ayenera kuti anakhala m’mayiko omwe anachokerawo kwa moyo wawo wonse. (Yer. 44:1) Choncho n’kutheka kuti ambiri mwa anthuwa ankalankhula komanso kuoneka ngati anthu a m’mayikowo, osati ngati Ayuda. Pamene anthu 3,000 ochokera m’mayiko enawa anabatizidwa, mpingo wachikhristu unakhala ndi anthu a mitundu yosiyanasiyana. Ngakhale kuti anthuwa anali osiyana, “tsiku ndi tsiku anali kusonkhana kukachisi mogwirizana.”​—Mac. 2:46.

Kodi mungasonyeze bwanji chidwi chenicheni kwa . . .

  • anthu a m’gawo lanu amene anachokera m’mayiko ena?

  • abale ndi alongo a mumpingo wanu omwe anachokera m’mayiko ena?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena