Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 March tsamba 4
  • Esau Anagulitsa Ukulu Wake

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Esau Anagulitsa Ukulu Wake
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mumayamikira Zinthu Zopatulika?
    Nsanja ya Olonda—1988
  • Muzisankha Zinthu Mwanzeru Kuti Musataye Madalitso Anu
    Nsanja ya Olonda—2013
  • Yakobo Analandira Madalitso
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Anthu Okonda Yehova Amasankha Zinthu Mwanzeru
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2024
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 March tsamba 4
M’bale akusinkhasinkha zimene wawerenga m’Baibulo. Akuganizira kuti akuona Esau akugulitsa ukulu wake kwa Yakobo pousinthanitsa ndi mbale ya mphodza.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 25-26

Esau Anagulitsa Ukulu Wake

25:27-34

Esau ‘sanayamikire zinthu zopatulika.’ (Ahe 12:16) Iye anagulitsa ukulu wake ndipo kenako anakwatira akazi awiri achikunja.​—Ge 26:34, 35.

DZIFUNSENI KUTI: ‘Kodi ndingasonyeze bwanji kuti ndimayamikira zinthu zopatulika zotsatirazi?’

  • Ubwenzi wanga ndi Yehova

  • Mzimu woyera

  • Kudziwika ndi dzina loyera la Yehova

  • Ntchito yolalikira

  • Misonkhano

  • Ukwati

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena