Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 July tsamba 4
  • Mose ndi Aroni Anasonyeza Kulimba Mtima Kwambiri

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mose ndi Aroni Anasonyeza Kulimba Mtima Kwambiri
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • Mafunso Ochokera kwa Owerenga
    Nsanja ya Olonda—2010
  • Mose ndi Aroni—Alengezi Olimba Mtima a Mawu a Mulungu
    Nsanja ya Olonda—1996
  • Mose ndi Aroni Aona Farao
    Bukhu Langa la Nkhani za Baibulo
  • Kodi ‘Mukuona Wosaonekayo’?
    Nsanja ya Olonda—2014
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 July tsamba 4
Mose ndi Aroni akuonekera kwa Farao amene wakhala pa mpando wake wachifumu.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | EKISODO 10-11

Mose ndi Aroni Anasonyeza Kulimba Mtima Kwambiri

10:3-6, 24-26, 28; 11:4-8

Mose ndi Aroni anasonyeza kulimba mtima kwambiri pamene ankayankhula ndi Farao, yemwe pa nthawiyo anali mfumu yamphamvu kwambiri padziko lonse lapansi. Kodi n’chiyani chinawathandiza? Ponena za Mose, Baibulo limati: “Mwa chikhulupiriro anachoka mu Iguputo, koma osati chifukwa choopa mfumu ayi, pakuti anapitiriza kupirira moleza mtima ngati kuti akuona Wosaonekayo.” (Ahe 11:27) Mose ndi Aroni ankakhulupirira kwambiri Yehova ndipo ankamudalira.

Kodi ndi zochitika ziti zomwe zingafune kuti mulimbe mtima kuti mufotokoze zimene mumakhulupirira kwa munthu waudindo?

Zithunzi zosonyeza zochitika zomwe zingafune kulimba mtima: 1. Mnyamata kusukulu wangoima pamene anzake akuchitira sailuti mbendera. 2. M’bale ali m’khoti pamaso pa oweruza. 3. M’bale wachinyamata akupereka kapepala kwa mwininyumba ndipo wapolisi yemwe ali chapafupi akumuyang’anitsitsa.
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena