Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 August tsamba 1
  • Zimene Tinganene

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Tinganene
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • ●○ ULENDO WOYAMBA
  • ○● ULENDO WOBWEREZA
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Zimene Tinganene
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Zimene Tinganene
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 August tsamba 1
Mose wakweza manja ake ndipo akulekanitsa Nyanja Yofiira. Aisiraeli komanso anthu ena ambiri omwe si Aisiraeli akuyang’ana modabwa.

Mose watambasula dzanja lake kuti alekanitse madzi pa Nyanja Yofiira

Zimene Tinganene

●○ ULENDO WOYAMBA

Funso: Kodi tingapeze kuti mfundo zimene zingatithandize tikaferedwa?

Lemba: 2Ak 1:3, 4

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi chimachitika n’chiyani munthu akamwalira?

LEMBALI LIKUPEZEKA MU:

  • Buku lakuti ‘Zimene Baibulo Limaphunzitsa’

    bhs 71 ¶4

○● ULENDO WOBWEREZA

Funso: Kodi chimachitika n’chiyani munthu akamwalira?

Lemba: Mla 9:5, 10

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi anthu amene anamwalira angadzakhalenso ndi moyo?

LEMBALI LIKUPEZEKA MU:

  • Buku lakuti ‘Zimene Baibulo Limaphunzitsa’

    bhs 63 ¶6

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena