Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 September tsamba 2
  • Musamatsatire Khamu la Anthu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Musamatsatire Khamu la Anthu
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • Khamu Lalikulu la Anthu Likudalitsidwa ndi Yehova
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Muzikhala Okonzeka Kukhululuka
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Miseche Kodi Nchifukwa Ninji Imasangalatsa?
    Galamukani!—1991
  • Khamu Lalikulu Kwambiri
    Mapeto Osangalatsa a Masomphenya a M’buku la Chivumbulutso
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 September tsamba 2
Anthu akuonera nyuzi pa mafoni awo komanso pa TV yaikulu m’malo opezeka anthu ambiri.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | EKISODO 23-24

Musamatsatire Khamu la Anthu

23:1-3

Yehova anachenjeza mboni komanso oweruza milandu kuti asamatengeke ndi khamu la anthu kuti apereke umboni wonama kapena kuweruza mopanda chilungamo. Mfundo imeneyi ingatithandizenso pochita zinthu zambiri. Tikutero chifukwa chakuti nthawi zonse Akhristu akufunika kuyesetsa kuti asatengere maganizo komanso makhalidwe oipa am’dzikoli.​—Aro 12:2.

N’chifukwa chiyani si nzeru kutsatira khamu la anthu pamene

  • tamva nkhani zopanda umboni kapena miseche?

  • tikusankha zovala, masitayilo a tsitsi kapena zosangalatsa?

  • tikuganizira kapena kuchita zinthu ndi anthu amtundu wina, chikhalidwe china kapena amene timasiyana nawo pa nkhani ya chuma?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena