Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 November tsamba 4
  • Muzipereka kwa Yehova Zonse Zimene Mungathe

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzipereka kwa Yehova Zonse Zimene Mungathe
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • Muzipereka Zinthu Zabwino Kwambiri kwa Yehova
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • “Ine Ndidzakhala Nawe Polankhula”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nsembe Zotamanda Zimene Zimakondweretsa Yehova
    Nsanja ya Olonda—2000
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
    Galamukani!—2022
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 November tsamba 4
Yehova akulandira nsembe zosiyanasiyana zoperekedwa ndi Aisiraeli. 1. Ufa wosalala. 2. Njiwa. 3. Banja likupititsa nkhosa kwa wansembe.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | LEVITIKO 4-5

Muzipereka kwa Yehova Zonse Zimene Mungathe

5:5-7, 11

Kukhala osauka sikunkalepheretsa Aisiraeli kukhala pa mtendere ndi Yehova. Ngakhale Aisiraeli osauka kwambiri ankatha kupereka chopereka chovomerezeka kwa Yehova ngati zimene anaperekazo zinali zonse zimene akanakwanitsa. Iwo ankatha kupereka ufa koma Yehova ankafuna kuti ukhale “wosalala,” womwe ankaugwiritsa ntchito akalandira alendo olemekezeka. (Ge 18:6) Masiku anonso, Yehova amalandira ‘nsembe yathu yachitamando’ ngati tikupereka zonse zimene tingathe. Iye amalandira ngakhale kuti ndi zochepa chifukwa cha mmene zinthu zilili pa moyo wathu.—Ahe 13:15.

Kodi zimenezi zingakulimbikitseni bwanji ngati simungathe kuchita zimene munkachita poyamba, mwina chifukwa cha matenda kapena uchikulire?

Alongo awiri akupereka ‘nsembe yachitamando’ kwa Yehova. 1. Mlongo amene akutumikira kudziko lina akulankhula ndi mzimayi pamsika. 2. Mlongo wachikulire akulemba makalata ali kunyumba kwake.
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena